Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Mapazi a okhulupirika ake amawateteza.+

      Koma anthu oipa amawawononga mu mdima,+

      Pakuti munthu sakhala wapamwamba chifukwa cha mphamvu zake.+

  • Salimo 30:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Imbani nyimbo zotamanda Yehova, inu okhulupirika ake,+

      Yamikani dzina lake loyera.*+

  • Salimo 132:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Ansembe anu avale chilungamo,+

      Ndipo okhulupirika anu afuule mosangalala.+

  • Salimo 149:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Anthu okhulupirika akondwere mu ulemerero.

      Iwo aimbe mosangalala pamabedi awo.+

  • Aheberi 13:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kudzera mwa iye, tiyeni nthawi zonse tizitamanda Mulungu. Tizichita zimenezi monga nsembe imene tikupereka kwa Mulungu,+ yomwe ndi chipatso cha milomo yathu.+ Timagwiritsa ntchito milomo imeneyi polengeza dzina lake kwa anthu ena.+

  • 1 Petulo 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 inunso monga miyala yamoyo mukumangidwa n’kukhala nyumba yauzimu+ kuti mudzakhale ansembe oyera, n’cholinga chakuti mupereke nsembe zauzimu+ zovomerezeka pamaso pa Mulungu kudzera mwa Yesu Khristu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena