Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 34:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Ndidzatamanda Yehova nthawi zonse.+

      Ndidzamutamanda ndi pakamwa panga mosalekeza.+

  • Salimo 51:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Inu Yehova, tsegulani milomo yangayi,+

      Kuti pakamwa panga patamande inu.+

  • Salimo 71:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 M’kamwa mwanga mwadzaza mawu otamanda inu,+

      Ndipo pakamwa panga pakunena za ulemerero wanu tsiku lonse.+

  • Salimo 89:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 89 Ndidzaimba mpaka kalekale za ntchito za Yehova zosonyeza kukoma mtima kwake kosatha.+

      Ndidzalengeza ndi pakamwa panga ku mibadwomibadwo za kukhulupirika kwanu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena