Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 15:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndi amene akuyenda mosalakwitsa zinthu,+ amene amachita chilungamo,+

      Ndi kulankhula zoona mumtima mwake.+

  • Salimo 24:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Aliyense wopanda mlandu m’manja mwake ndi woyera mumtima mwake,+

      Amene sanaone Moyo wanga ngati wopanda pake,+

      Kapena kulumbira mwachinyengo.+

  • Salimo 25:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ubwenzi wolimba ndi Yehova ndi wa anthu amene amamuopa,+

      Pangano lakenso ndi la anthu oterowo, ndipo iye amawadziwitsa panganolo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena