Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 26:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Patapita nthawi ali kumeneko, Abimeleki mfumu ya Afilisiti anali kuyang’ana pawindo, ndipo anaona Isaki akucheza mwachikondi ndi mkazi wake Rabeka.+

  • Genesis 29:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Yakobo anagwira ntchito zaka 7 kuti atenge Rakele.+ Koma iye anangoziona zakazo ngati masiku ochepa chabe, chifukwa anam’konda kwambiri mtsikanayo.+

  • Nyimbo ya Solomo 8:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Undiike pamtima pako ngati chidindo,+ ndiponso undiike ngati chidindo padzanja lako, chifukwa chikondi n’champhamvu ngati imfa.+ Mofanana ndi Manda,* chikondi sichigonja ndipo chimafuna kudzipereka ndi mtima wonse.+ Kuyaka kwake kuli ngati kuyaka kwa moto. Chikondicho ndi lawi la Ya.*+

  • Aefeso 5:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Amuna inu, pitirizani kukonda akazi anu+ monga mmene Khristu anakondera mpingo n’kudzipereka yekha chifukwa cha mpingowo,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena