Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 32:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Anthu inu, musakhale ngati hatchi kapena nyulu* yosazindikira,+

      Imene munthu amachita kuimanga chingwe chapakamwa ndi chapamutu kuti athetse kupulupudza kwake,+

      Ndi kuti aiyandikire.”+

  • Miyambo 19:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Zilango anazikhazikitsira anthu onyoza,+ ndipo zikwapu anazisungira msana wa anthu opusa.+

  • Miyambo 26:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Chikwapu n’cha hatchi,+ zingwe n’za pakamwa pa bulu,+ ndipo ndodo ndi yokwapulira msana wa anthu opusa.+

  • 1 Akorinto 4:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Kodi mukufuna chiyani? Mukufuna ndibwere kwa inu ndi chikwapu,+ kapena ndi chikondi ndi mzimu wofatsa?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena