Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 31:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Kodi si paja wochita zoipa amakumana ndi zosautsa,+

      Ndipo ochitira anzawo zopweteka tsoka limawagwera?

  • Salimo 1:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Pakuti Yehova amadziwa njira za olungama,+

      Koma oipa adzatheratu pamodzi ndi njira zawo.+

  • Luka 13:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Koma iye adzakuuzani kuti, ‘Sindikudziwa kumene mukuchokera. Ndichokereni pano, nonsenu ochita zinthu zosalungama!’+

  • Aroma 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Koma adzapereka chilango ndi mkwiyo+ kwa okonda mikangano+ amenenso samvera choonadi+ koma amamvera zosalungama.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena