Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 31:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Koma bambo anu akhala akundipusitsa, ndipo asintha malipiro anga maulendo 10. Ngakhale ndi choncho, Mulungu sanawalole kuti andichite choipa.+

  • Yeremiya 39:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 “‘Pakuti ine ndidzakupulumutsa ndithu, ndipo sudzaphedwa ndi lupanga, koma udzapulumutsa moyo wako+ chifukwa chakuti wandikhulupirira,’+ watero Yehova.”

  • Yeremiya 40:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Tsopano taona! Lero ndakumasula maunyolo amene anali m’manja mwako. Ngati ungakonde kutsagana nane ku Babulo tiye, ndipo ndidzakuyang’anira.+ Koma ngati sungakonde kutsagana nane ku Babulo, tsala. Taona! Dziko lonse lili pamaso pako. Pita kulikonse kumene ungaone kuti n’kwabwino, kulikonse kumene ungakonde kupita.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena