Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 8:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 M’makalatawo mfumu inalola Ayuda amene anali m’mizinda yosiyanasiyana kuti asonkhane+ ndi kuteteza miyoyo yawo. Inawalolanso kuwononga, kupha ndi kufafaniza magulu onse ankhondo a anthu+ ndi zigawo zimene zinali kuwachitira nkhanza, ngakhalenso ana ndi akazi ndiponso kufunkha zinthu zawo.+

  • Miyambo 10:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Zoyembekezera za olungama zimasangalatsa,+ koma chiyembekezo cha oipa chidzawonongeka.+

  • Danieli 3:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Tsopano masatarapi, akuluakulu a boma, abwanamkubwa, ndi nduna zapamwamba+ za mfumu zimene zinasonkhana zinaonadi kuti motowo sunavulaze amuna amphamvu amenewa,+ ndipo tsitsi lawo silinawauke ndi limodzi lomwe.+ Zovala zawo sizinasinthe ndipo sanali kumveka ngakhale fungo la moto.

  • Danieli 6:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Pamenepo mfumuyo inasangalala kwambiri+ ndipo inalamula kuti Danieli amutulutse m’dzenjemo. Danieli anatulutsidwadi m’dzenjelo ndipo sanavulale paliponse chifukwa anakhulupirira Mulungu wake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena