Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 141:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Nditetezeni kuti ndisagwidwe pamsampha umene anditchera,+

      Kuti ndisakodwe ndi makhwekhwe a anthu ochita zopweteka anzawo.+

  • Salimo 142:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Mvetserani kulira kwanga kochonderera,+

      Pakuti ndasautsika koopsa.+

      Ndipulumutseni kwa anthu amene akundizunza,+

      Pakuti iwo ndi amphamvu kuposa ine.+

  • Aroma 8:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Tikudziwa tsopano kuti Mulungu amagwirizanitsa zochita zake zonse+ pofuna kupindulitsa amene amakonda Mulungu, anthu oitanidwa mogwirizana ndi cholinga chake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena