Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Danieli 10:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Sindinadye chakudya chokoma, sindinadye nyama kapena kumwa vinyo ndipo sindinadzole mafuta kufikira milungu itatu yonseyo itatha.+

  • Mateyu 6:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Koma iwe, pamene ukusala kudya, dzola mafuta m’mutu mwako ndi kusamba nkhope yako,+

  • Luka 7:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Iwe sunathire mafuta m’mutu mwanga,+ koma mayiyu wapaka mapazi anga mafuta onunkhira.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena