Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 10:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Munandiveka khungu ndiponso mnofu,

      Ndipo munandiluka ndi mafupa ndi mitsempha.+

  • Salimo 139:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Inu munapanga impso zanga,+

      Ndipo munali kunditchinga m’mimba mwa mayi anga.+

  • Salimo 139:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mafupa anga sanali obisika kwa inu+

      Pamene munali kundipanga m’malo obisika,+

      Pamene munali kundiwomba ngati nsalu m’malo apansi kwambiri+ padziko lapansi.

  • Yeremiya 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Ndisanakuumbe m’mimba,+ ndinakudziwa,+ ndipo usanatuluke m’mimbamo, ndinakusankha kuti uchite ntchito yopatulika.+ Ndinakusankha kuti ukhale mneneri ku mitundu ya anthu.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena