Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 20:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Bwerera, kauze Hezekiya mtsogoleri+ wa anthu anga kuti, ‘Yehova Mulungu+ wa Davide kholo lako wanena kuti: “Ndamva+ pemphero lako,+ ndipo ndaona misozi yako.+ Ndikuchiritsa.+ Pa tsiku lachitatu udzapita kunyumba ya Yehova.+

  • Salimo 39:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Imvani pemphero langa, inu Yehova,

      Ndipo tcherani khutu pamene ndikufuula kupempha thandizo.+

      Musandinyalanyaze pamene ndikugwetsa misozi.+

      Pakuti ndine mlendo wanu,+

      Mlendo wokhala nanu monga anachitira makolo anga onse.+

  • Salimo 56:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Inu mwalemba za kuthawathawa kwanga.+

      Sungani misozi yanga m’thumba lanu lachikopa.+

      Kodi misozi yanga sili m’buku lanu?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena