Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 8:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pamenepo Farao anayankha kuti: “Mawa.” Ndiyeno Mose anati: “Zidzachitika monga mwa mawu anu, kuti mudziwe kuti palibenso wina wofanana ndi Yehova Mulungu wathu,+

  • 1 Samueli 2:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Palibe woyera ngati Yehova. Palibe aliyense koma inu nokha.+

      Palibe thanthwe lofanana ndi Mulungu wathu.+

  • Salimo 86:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Inu Yehova, palibe mulungu wina amene angafanane ndi inu.+

      Ndipo palibe ntchito zilizonse zofanana ndi ntchito zanu.+

  • Salimo 89:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Pakuti ndani kumwamba angayerekezeredwe ndi Yehova?+

      Ndani angafanane ndi Yehova pakati pa ana a Mulungu?+

  • Salimo 113:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ndani angafanane ndi Yehova Mulungu wathu,+

      Amene amakhala pamwamba?+

  • Yeremiya 10:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Ndithudi palibe aliyense wofanana ndi inu Yehova.+ Inu ndinu wamkulu, ndipo dzina lanu ndi lalikulu ndi lamphamvu.+

  • Mika 7:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kodi pali Mulungu winanso wofanana ndi inu+ amene amakhululukira zolakwa+ ndi machimo a anthu ake otsala omwe ndi cholowa chake?+ Inu simudzakhalabe wokwiya mpaka kalekale, pakuti kusonyeza kukoma mtima kosatha kumakusangalatsani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena