Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 30:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Lamulo limene ndikukupatsa lero si lovuta kwa iwe kulitsatira, ndipo si lapatali.+

  • Miyambo 8:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Nzerutu ikungokhalira kufuula,+ ndipo kuzindikira kukungokhalira kutulutsa mawu.+

  • Yesaya 48:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Bwerani pafupi ndi ine anthu inu. Mvetserani izi. Kuyambira pa chiyambi, ine sindinalankhulirepo m’malo obisika.+ Pamene zinthu zonenedwazo zinayamba kuchitika, ine ndinalipo.”

      Tsopano Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, watumiza ine ndiponso watumiza mzimu wake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena