-
Ezara 9:9Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
9 Ngakhale kuti ndife akapolo,+ Mulungu wathu sanatisiye mu ukapolo wathuwo,+ koma watisonyeza kukoma mtima kosatha pamaso pa mafumu a ku Perisiya.+ Wachita zimenezi kuti atitsitsimutse n’cholinga choti tikamange nyumba ya Mulungu wathu+ komanso tikakonze malo ozungulira nyumbayo amene anali bwinja,+ ndi kuti tikhale mu Yuda ndi mu Yerusalemu ngati kuti tili mumpanda wamiyala.+
-