Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 91:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Adzakutchinjiriza ndi mapiko ake,+

      Udzathawira pansi pa mapiko ake.+

      Choonadi chake+ chidzakhala chishango chako+ chachikulu ndi malo ako achitetezo.

  • Yeremiya 23:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Ndidzapatsa nkhosazo abusa ndipo adzaziweta.+ Sizidzaopanso kanthu kapena kugwidwa ndi mantha aakulu,+ ndipo palibe imene idzasowa,” watero Yehova.

  • Zefaniya 3:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Otsala mwa Isiraeli+ sadzachita zinthu zosalungama+ kapena kunena bodza.+ Sadzakhala ndi lilime lachinyengo+ koma iwo adzadya ndi kugona pansi momasuka+ ndipo sipadzakhala wowaopsa.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena