Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mbiri 16:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Choncho anamuika m’manda ake olemekezeka kwambiri,+ amene iye anadzikumbira mu Mzinda wa Davide.+ Pomuika m’mandamo, anamugoneka pabedi pomwe anathirapo mafuta a basamu ambiri+ ndi msakanizo wapadera wa mafuta onunkhira.+ Kuwonjezera apo, pamaliro ake anapserezapo zofukiza+ zochuluka kwambiri.

  • Yesaya 14:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Mafumu ena onse a mitundu ya anthu anagona pansi mu ulemerero, aliyense m’manda ake.+

  • Ezekieli 32:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Bedi lake aliika pakati pa anthu ophedwa,+ aliika pakati pa khamu lake lonse. Manda a anthu ake azungulira bedilo. Onsewo ndi anthu osadulidwa, ophedwa ndi lupanga+ chifukwa anachititsa mantha anthu m’dziko la anthu amoyo. Adzanyozeka limodzi ndi amene akutsikira kudzenje. Iye waikidwa m’manda pakati pa anthu ophedwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena