Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 36:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Inu Mulungu, kukoma mtima kwanu kosatha ndi kwamtengo wapatali!+

      Ndipo ana a anthu amabisala mu mthunzi wa mapiko anu.+

  • Salimo 37:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Komanso sangalala mwa Yehova,+

      Ndipo adzakupatsa zokhumba za mtima wako.+

  • Habakuku 3:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ine ndidzakondwerabe mwa Yehova+ ndipo ndidzasangalala mwa Mulungu wachipulumutso changa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena