Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 25:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Iye adzameza imfa kwamuyaya+ ndipo Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, adzapukuta misozi pankhope zonse za anthu.+ Adzachotsa kunyozeka kwa anthu ake padziko lonse lapansi,+ pakuti Yehova ndiye wanena zimenezi.

  • Mateyu 5:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 “Odala ndi anthu amene akumva chisoni, chifukwa adzasangalatsidwa.+

  • Luka 6:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 “Inu amene mukumva njala+ tsopano ndinu odala, chifukwa mudzakhuta.+

      “Inu amene mukulira tsopano ndinu odala, chifukwa mudzaseka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena