Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 10:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 N’chifukwa chiyani inu Yehova mukuima kutali?+

      N’chifukwa chiyani mukubisala pa nthawi ya masautso?+

  • Salimo 74:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 N’chifukwa chiyani mwachotsa dzanja lanu, dzanja lanu lamanja,+

      Pachifuwa panu koma osachitapo kanthu? Kodi mukatero ife sitiwonongedwa?

  • Zekariya 1:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Choncho mngelo wa Yehova anati: “Inu Yehova wa makamu, kodi Yerusalemu ndi mizinda ya Yuda imene munaikana ndi kuisiya kwa zaka 70,+ simuichitira chifundo kufikira liti?”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena