Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Anayamba kusankha milungu yatsopano.+

      Atatero m’pamene nkhondo inafika m’mizinda.+

      Panalibe chishango kapena mkondo waung’ono,

      Pakati pa anthu 40,000 mu Isiraeli.+

  • Salimo 81:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Choncho ndinawasiya kuti apitirize kuumitsa mtima wawo.+

      Iwo anapitiriza kuyenda mu nzeru zawo.+

  • Yeremiya 14:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ponena za anthu awa Yehova wati: “Iwo akukonda kuyendayenda+ ndipo sanalamulire mapazi awo.+ Choncho Yehova sakukondwera nawo,+ moti adzakumbukira zolakwa zawo ndipo adzawalanga chifukwa cha machimo awo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena