Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 38:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Anthu amene akufuna kundiwononga anditchera misampha,+

      Amene akufuna kundivulaza akulankhula motsutsana nane,+

      Ndipo amakhala akukonza zachinyengo tsiku lonse.+

  • Salimo 64:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Amaumirira kulankhula zoipa,+

      Amakambirana kuti atchere misampha.+

      Iwo amati: “Angaione ndani?”+

  • Salimo 140:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Anthu odzikweza anditchera msampha.+

      Iwo aika zingwe ponseponse ngati ukonde m’mphepete mwa njira,+

      Ndipo anditchera makhwekhwe.+ [Seʹlah.]

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena