Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 10:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Mumtima mwake+ amanena kuti: “Mulungu waiwala zochita zanga.+

      Wabisa nkhope yake.+

      Ndithudi, sadzaona kalikonse.”+

  • Salimo 59:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Taonani! Amabwetuka ndi pakamwa pawo.+

      Milomo yawo ili ngati malupanga,+

      Pakuti iwo amati: “Ndani akumvetsera?”+

  • Salimo 94:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iwo amanena kuti: “Ya sakuona,+

      Ndipo Mulungu wa Yakobo sakudziwa zimene zikuchitika.”+

  • Ezekieli 8:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ndiyeno iye anandiuza kuti: “Iwe mwana wa munthu, kodi waona zimene akuluakulu a Isiraeli akuchita mu mdima?+ Kodi waona zimene aliyense wa iwo akuchita m’chipinda chamkati mmene muli fano lake losema? Iwo akunena kuti, ‘Yehova sakutiona.+ Yehova wachokamo m’dziko muno.’”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena