Numeri 3:32 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 32 Mkulu wa atsogoleri onse a Alevi anali Eleazara,+ mwana wa wansembe Aroni. Iye ndiye anali kuyang’anira onse otumikira pamalo oyera. Numeri 4:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 “Eleazara mwana wa wansembe Aroni, aziyang’anira+ mafuta+ a nyale, zofukiza zonunkhira,+ nsembe yanthawi zonse yambewu,+ ndi mafuta odzozera.+ Aziyang’aniranso chihema chonse chopatulika ndi zonse za mmenemo, ndiwo malo oyerawo ndi ziwiya zake.” Yeremiya 20:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Tsopano Pasuri, mwana wa Imeri,+ wansembe, amenenso anali mtumiki wamkulu panyumba ya Yehova,+ anakhala tcheru kumvetsera pamene Yeremiya anali kulosera mwa kunena mawu amenewa.
32 Mkulu wa atsogoleri onse a Alevi anali Eleazara,+ mwana wa wansembe Aroni. Iye ndiye anali kuyang’anira onse otumikira pamalo oyera.
16 “Eleazara mwana wa wansembe Aroni, aziyang’anira+ mafuta+ a nyale, zofukiza zonunkhira,+ nsembe yanthawi zonse yambewu,+ ndi mafuta odzozera.+ Aziyang’aniranso chihema chonse chopatulika ndi zonse za mmenemo, ndiwo malo oyerawo ndi ziwiya zake.”
20 Tsopano Pasuri, mwana wa Imeri,+ wansembe, amenenso anali mtumiki wamkulu panyumba ya Yehova,+ anakhala tcheru kumvetsera pamene Yeremiya anali kulosera mwa kunena mawu amenewa.