Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 10:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Chotero iwo ananyamuka kuphiri la Yehova,+ n’kuyenda ulendo wa masiku atatu. Likasa la pangano la Yehova+ linali patsogolo pawo ulendo wa masiku atatu wonsewo, kuwafunira malo oti amangepo msasa.+

  • Salimo 95:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kunena za anthu amenewa ndinalumbira mu mkwiyo wanga kuti:+

      “Sadzalowa mu mpumulo wanga.”+

  • Yesaya 63:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Monga momwe chilombo chakutchire chimatsetserekera kuchigwa, mzimu wa Yehova unawapumitsa.”+

      Chotero inu munatsogolera anthu anu kuti mudzipangire dzina lokongola.+

  • Aheberi 4:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Pakuti ngati Yoswa+ anawalowetsa m’malo ampumulo,+ Mulungu sakananenanso pambuyo pake+ za tsiku lina.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena