Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:43
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 43 Kondwerani, mitundu inu, pamodzi ndi anthu ake,+

      Pakuti adzabwezera magazi a atumiki ake,+

      Ndipo adzabwezera chilango kwa adani ake,+

      Nadzaphimba machimo a dziko la anthu ake.”

  • Salimo 96:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Lengezani ulemerero wake pakati pa anthu a mitundu ina,+

      Ndiponso ntchito zake zodabwitsa pakati pa mitundu yonse ya anthu.+

  • Yesaya 44:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 “Fuulani mokondwa kumwamba inu,+ pakuti Yehova wachitapo kanthu.+ Fuulani mosangalala,+ inu malo otsika kwambiri a dziko lapansi.+ Mapiri+ inu ndiponso iwe nkhalango ndi inu mitengo yonse ili mmenemo, kondwani ndi kufuula ndi chisangalalo. Pakuti Yehova wawombola Yakobo ndipo wasonyeza kukongola kwake pa Isiraeli.”+

  • Aroma 15:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Komanso Malemba amati: “Kondwerani, mitundu inu, pamodzi ndi anthu ake.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena