Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yesaya 12:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Muimbireni nyimbo Yehova+ chifukwa wachita zopambana.+ Zimenezi zikulengezedwa m’dziko lonse lapansi.

  • Amosi 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “‘Lengezani izi pansanja zokhalamo za ku Asidodi ndi pansanja zokhalamo za m’dziko la Iguputo.+ Munene kuti: “Sonkhanani pamodzi kuti muukire mapiri a Samariya+ ndipo onani zinthu zambiri zachisokonezo ndi zachinyengo zimene zikuchitika mumzinda umenewo.+

  • Machitidwe 26:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Zolembazo zinaneneratu kuti Khristu adzavutika,+ ndipo monga woyamba kuukitsidwa kwa akufa,+ iye adzafalitsa kuwala+ mwa anthu awa ndi kwa anthu a mitundu ina.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena