Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 38:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Kodi malamulo akuthambo ukuwadziwa,+

      Kapena kodi ulamuliro wake ungauike padziko lapansi?

  • Salimo 74:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Usana ndi wanu, usikunso ndi wanu.+

      Inu munapanga chounikira, munapanga dzuwa.+

  • Salimo 104:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Wapanga mwezi kuti uzisonyeza nthawi yoikidwiratu.+

      Dzuwa nalo limadziwa bwino kumene limalowera.+

  • Yeremiya 31:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Yehova ndiye Wopereka dzuwa kuti liziwala masana,+ woikira mwezi malamulo,+ wopereka nyenyezi+ kuti ziziwala usiku,+ amene amavundula nyanja kuti mafunde ake achite phokoso.+ Wochita zimenezi dzina lake ndi Yehova wa makamu.+ Iye wanena kuti:

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena