Salimo 50:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Iwe umadana ndi malangizo,*+Ndipo umaponya mawu anga kunkhongo.+ Yesaya 28:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Chotero imvani mawu a Yehova inu anthu odzitama, inu atsogoleri+ a anthu awa amene muli mu Yerusalemu:
14 Chotero imvani mawu a Yehova inu anthu odzitama, inu atsogoleri+ a anthu awa amene muli mu Yerusalemu: