Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ezekieli 32:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 “‘Ndikadzasandutsa dziko la Iguputo bwinja ndipo zinthu zonse za m’dzikolo zikadzawonongedwa,+ komanso ndikadzapha anthu onse okhala m’dzikolo, anthu a mitundu ina adzadziwa kuti ine ndine Yehova.+

  • Zefaniya 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “Tsoka kwa anthu okhala m’chigawo cha m’mphepete mwa nyanja, mtundu wa Akereti.+ Yehova wakudzudzulani anthu inu. Iwe Kanani, dziko la Afilisiti, nawenso ndidzakuwononga, kotero kuti m’dziko lako simudzatsala munthu aliyense.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena