Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 21:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Choncho tiyeni tiwalase.

      Ndithu Hesiboni adzafafanizika mpaka ku Diboni,+

      Amayi adzaphedwa mpaka ku Nofa, amuna mpaka ku Medeba.”+

  • Yoswa 13:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Hesiboni,+ ndi midzi yake yonse+ imene inali m’malo okwererapowo. Linaphatikizaponso Diboni,+ Bamoti-baala,+ Beti-baala-meoni,+

  • Yesaya 15:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Iye wapita kukachisi ndi ku Diboni.+ Wapita kumalo okwezeka kukalira. Mowabu akulira mofuula chifukwa cha Nebo+ ndi Medeba.+ Anthu onse a mmenemo ameta mipala.+ Ndevu za munthu aliyense zametedwa.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena