Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 10:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Kuchoka pamenepo upitirize ulendo wako mpaka kukafika kumtengo waukulu wa ku Tabori. Kumeneko ukumana ndi amuna atatu akupita ku Beteli+ kukapembedza Mulungu woona. Mmodzi wa iwo akhala atanyamula ana atatu a mbuzi,+ wina atanyamula mitanda yobulungira itatu ya mkate,+ ndipo winayo atanyamula mtsuko waukulu wa vinyo.+

  • 1 Samueli 25:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Nthawi yomweyo, Abigayeli+ anafulumira kutenga mitanda 200 ya mkate, mitsuko iwiri ikuluikulu ya vinyo,+ anapha nkhosa zisanu,+ anatenganso miyezo ya seya* isanu ya tirigu wokazinga,+ mphesa zouma zoumba pamodzi 100+ ndi nkhuyu zouma zoumba pamodzi 200+ ndi kuzikweza pa abulu.

  • 2 Samueli 16:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Davide atapitirira pang’ono pamwamba pa phiri paja,+ anaona Ziba+ mtumiki wa Mefiboseti+ akubwera kudzakumana naye. Iye anali ndi abulu awiri+ okhala ndi zishalo ndipo abuluwa anali atanyamula mitanda 200 ya mkate,+ mphesa zouma zoumba pamodzi 100,+ zipatso za m’chilimwe* 100+ zouma zoumba pamodzi ndiponso mtsuko waukulu wa vinyo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena