Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Koma Yehova adzakhala pampando wachifumu mpaka kalekale,+

      Adzakhazikitsa mpando wake wachifumu kuti aweruze.+

  • Salimo 90:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mapiri asanabadwe,+

      Kapena musanakhazikitse dziko lapansi+ ndi malo okhalapo anthu,*+

      Inu ndinu Mulungu kuyambira kalekale mpaka kalekale.+

  • Salimo 102:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Koma inu Yehova, mudzakhalapobe kwamuyaya,+

      Dzina lanu* lidzakhalapobe ku mibadwomibadwo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena