Salimo 9:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Anthu oipa+ adzapita ku Manda,+Ngakhalenso anthu onse a mitundu ina amene aiwala Mulungu.+ Salimo 55:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Chiwonongeko chiwagwere!+Atsikire ku Manda ali amoyo.+Pakuti kulikonse kumene apita, zinthu zoipa zimakhala mumtima mwawo.+
15 Chiwonongeko chiwagwere!+Atsikire ku Manda ali amoyo.+Pakuti kulikonse kumene apita, zinthu zoipa zimakhala mumtima mwawo.+