Deuteronomo 32:15 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 15 Yesuruni*+ atayamba kunenepa, anayamba kupanduka.+Iwe wanenepa, wakulupala, wakhuta mopitirira muyezo.+Pamenepo iye anasiya Mulungu amene anam’panga,+Ndi kunyoza Thanthwe+ la chipulumutso chake. Yesaya 10:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Chotero Ambuye woona, Yehova wa makamu azidzatumizira anthu ake* onenepa nthenda yowondetsa,+ ndipo pansi pa ulemerero wake pazidzangoyaka, ngati kuyaka kwa moto.+ Amosi 4:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 “Tamverani mawu awa, inu ng’ombe zazikazi za ku Basana,+ zokhala m’phiri la Samariya,+ inu amene mukuchitira zachinyengo anthu onyozeka,+ amene mukuphwanya anthu osauka ndipo mukuuza ambuye anu kuti, ‘Tipatseni chakumwa kuti timwe!’
15 Yesuruni*+ atayamba kunenepa, anayamba kupanduka.+Iwe wanenepa, wakulupala, wakhuta mopitirira muyezo.+Pamenepo iye anasiya Mulungu amene anam’panga,+Ndi kunyoza Thanthwe+ la chipulumutso chake.
16 Chotero Ambuye woona, Yehova wa makamu azidzatumizira anthu ake* onenepa nthenda yowondetsa,+ ndipo pansi pa ulemerero wake pazidzangoyaka, ngati kuyaka kwa moto.+
4 “Tamverani mawu awa, inu ng’ombe zazikazi za ku Basana,+ zokhala m’phiri la Samariya,+ inu amene mukuchitira zachinyengo anthu onyozeka,+ amene mukuphwanya anthu osauka ndipo mukuuza ambuye anu kuti, ‘Tipatseni chakumwa kuti timwe!’