-
Ezekieli 38:16Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
16 Ndithu iwe udzabwera ngati mitambo kudzaphimba dzikolo ndi kudzaukira anthu anga Aisiraeli.+ Zimenezi zidzachitika m’masiku otsiriza, ndipo ine ndidzakubweretsa kuti uukire dziko langa.+ Ndidzachita izi kuti anthu a mitundu ina adzandidziwe pamene ndidzadziyeretse pamaso pawo, kudzera mwa iwe Gogi.”’+
-
-
Malaki 1:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 “Kuchokera kotulukira dzuwa kukafika kumene limalowera, dzina langa lidzakwezeka pakati pa anthu a mitundu ina.+ Kulikonse anthu azidzapereka nsembe zautsi.+ Anthu azidzapereka zopereka kapena kuti mphatso zovomerezeka polemekeza dzina langa.+ Adzachita izi chifukwa dzina langa lidzakhala lokwezeka pakati pa anthu a mitundu ina,”+ watero Yehova wa makamu.
-