Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 28:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “‘Koma pa tsiku la sabata,+ muzipereka nsembe ana a nkhosa awiri amphongo opanda chilema. Muziwapereka pamodzi ndi ufa wosalala monga nsembe yambewu. Ufawo muziuthira mafuta, ndipo uzikhala wokwana magawo awiri mwa magawo 10 a muyezo wa efa. Muziperekanso nsembe yake yachakumwa.

  • Ezekieli 45:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Mtsogoleri+ wa anthu adzapatsidwa udindo woyang’anira nsembe zopsereza zathunthu,+ nsembe yambewu+ ndi nsembe yachakumwa.+ Iye azidzayang’anira nsembezo pa nthawi ya zikondwerero,+ pa masiku okhala mwezi,+ pa nthawi ya masabata+ ndi pa nthawi ya zikondwerero zonse za nyumba ya Isiraeli.+ Mtsogoleriyo ndi amene azidzapereka kwa ansembe nyama za nsembe yamachimo, nsembe yambewu, nsembe yopsereza yathunthu ndi nsembe zachiyanjano kuti aphimbe machimo a nyumba ya Isiraeli.’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena