Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 29:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 “Kenako utenge nkhosa yowalongera unsembe ndi kuwiritsa nyama yake m’malo oyera.+

  • 2 Mbiri 35:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kenako anaphika+ nsembe ya pasika+ pamoto malinga ndi mwambo wawo ndipo zinthu zopatulika anaziphika+ m’miphika, m’miphika ya pansi pozungulira ndi m’miphika yosalowa kwambiri. Atatero anapititsa nyamayo msangamsanga kwa ana onse a anthuwo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena