Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 119:53
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  53 Mkwiyo ukuyaka mumtima mwanga chifukwa cha oipa,+

      Amene akusiya chilamulo chanu.+

  • Salimo 119:136
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 136 Misozi yatsika m’maso mwanga ngati mitsinje ya madzi,+

      Chifukwa chakuti iwo sanasunge chilamulo chanu.+

  • 2 Akorinto 12:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Mwina ndikadzabweranso, Mulungu wanga adzandichititsa manyazi pakati panu. Ndipo mwina ndidzalirira anthu ambiri amene anachimwa+ koma sanalape pa zonyansa zawo, dama*+ lawo, ndi khalidwe lawo lotayirira+ limene akhala akuchita.

  • 2 Petulo 2:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Munthu wolungama ameneyo anali kuzunzika tsiku ndi tsiku ndi zimene anali kuona ndi kumva pamene anali kukhala pakati pawo, ndiponso chifukwa cha zochita zawo zosamvera malamulo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena