Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 19:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Kenako anthu onse anayankhira pamodzi kuti: “Zonse zimene Yehova wanena tidzachita zomwezo.”+ Nthawi yomweyo Mose anatenga mawu a anthuwo ndi kubwerera nawo kwa Yehova.+

  • Levitiko 26:40
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 40 Chotero adzavomereza kuti iwo komanso makolo awo anayenda motsutsana nane,+ anandichimwira+ ndi kundichitira mosakhulupirika.

  • 1 Mafumu 11:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Ndichita zimenezi chifukwa iwo andisiya ine+ n’kuyamba kugwadira Asitoreti+ mulungu wamkazi wa Asidoni, Kemosi+ mulungu wa Amowabu, ndi Milikomu+ mulungu wa ana a Amoni. Sanayende m’njira zanga mwa kuchita choyenera pamaso panga ndi kutsatira malamulo anga ndi zigamulo zanga monga anachitira Davide bambo a Solomo.

  • Ezara 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Kuyambira masiku a makolo athu+ mpaka lero, takhala m’machimo aakulu kwambiri,+ ndipo chifukwa cha zolakwa zathu, ifeyo, mafumu athu,+ ndi ansembe athu,+ taperekedwa m’manja mwa mafumu a mayiko ena ndi lupanga,+ mwa kutengedwa ukapolo,+ kulandidwa katundu,+ komanso kukhala ndi nkhope zamanyazi+ ngati mmene tilili lero.

  • Nehemiya 9:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Mafumu athu, akalonga athu, ansembe athu ndi makolo athu+ sanatsatire chilamulo chanu+ ndipo sanamvere malamulo anu+ kapena zikumbutso zanu zowachenjeza.+

  • Ezekieli 20:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 chifukwa anakana zigamulo zanga, sanayende motsatira malamulo anga, anadetsa sabata langa komanso mtima wawo unali pa mafano awo onyansa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena