Yobu 19:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Dziwani kuti Mulungu mwiniwakeyo ndi amene wandisocheretsa,Ndipo wandizunguliza ndi ukonde wake wosakira nyama.+ Salimo 66:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Mwatilowetsa mu ukonde wosakira nyama,+Mwatinyamulitsa katundu wolemera m’chiuno mwathu. Yeremiya 52:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Kenako Akasidiwo anagwira mfumuyo n’kupita nayo ku Ribila,+ kwa mfumu ya Babulo,+ m’dziko la Hamati,+ kuti mfumu ya Babuloyo ikamuweruze.+ Maliro 1:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Iye watumiza moto m’mafupa+ mwanga kuchokera kumwamba, ndipo wafooketsa fupa lililonse.Watchera ukonde+ kuti ukole mapazi anga. Wandibweza kumbuyo.Wandisandutsa mkazi wosiyidwa popanda thandizo. Ndikudwala tsiku lonse.+ Ezekieli 17:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Ndidzam’ponyera ukonde wanga ndipo adzakodwa mu ukonde wanga wosakira.+ Ndiyeno ndidzamubweretsa ku Babulo ndi kumuweruza chifukwa chondichitira zinthu mosakhulupirika.+ Ezekieli 19:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Mitundu ya anthu a m’zigawo zonse zozungulira anabwera kudzauukira.+ Anauponyera ukonde+ wawo ndipo mkangowo unagwera m’mbuna zawo.+ Ezekieli 32:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Ndidzakuphimba ndi ukonde+ wanga pogwiritsa ntchito khamu la anthu ambiri a mitundu ina, ndipo iwo adzakukola ndi khoka langa.+ Hoseya 5:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 “Imvani inu ansembe+ ndipo mvetserani inu a m’nyumba ya Isiraeli. Inunso a m’nyumba ya mfumu+ mvetserani, pakuti chiweruzochi chikukhudza inuyo, chifukwa mwakhala msampha+ ku Mizipa ndipo mwakhala ngati ukonde paphiri la Tabori.+ Hoseya 7:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 “Kulikonse kumene iwo angapite, ndidzawatchera ndi ukonde.+ Ndidzawagwira ngati zolengedwa zouluka m’mlengalenga.+ Ndidzawalanga mogwirizana ndi chenjezo limene ndinauza msonkhano wawo.+ Luka 21:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 ngati msampha.+ Pakuti lidzafikira onse okhala pankhope ya dziko lonse lapansi.+
6 Dziwani kuti Mulungu mwiniwakeyo ndi amene wandisocheretsa,Ndipo wandizunguliza ndi ukonde wake wosakira nyama.+
9 Kenako Akasidiwo anagwira mfumuyo n’kupita nayo ku Ribila,+ kwa mfumu ya Babulo,+ m’dziko la Hamati,+ kuti mfumu ya Babuloyo ikamuweruze.+
13 Iye watumiza moto m’mafupa+ mwanga kuchokera kumwamba, ndipo wafooketsa fupa lililonse.Watchera ukonde+ kuti ukole mapazi anga. Wandibweza kumbuyo.Wandisandutsa mkazi wosiyidwa popanda thandizo. Ndikudwala tsiku lonse.+
20 Ndidzam’ponyera ukonde wanga ndipo adzakodwa mu ukonde wanga wosakira.+ Ndiyeno ndidzamubweretsa ku Babulo ndi kumuweruza chifukwa chondichitira zinthu mosakhulupirika.+
8 Mitundu ya anthu a m’zigawo zonse zozungulira anabwera kudzauukira.+ Anauponyera ukonde+ wawo ndipo mkangowo unagwera m’mbuna zawo.+
3 “Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti, ‘Ndidzakuphimba ndi ukonde+ wanga pogwiritsa ntchito khamu la anthu ambiri a mitundu ina, ndipo iwo adzakukola ndi khoka langa.+
5 “Imvani inu ansembe+ ndipo mvetserani inu a m’nyumba ya Isiraeli. Inunso a m’nyumba ya mfumu+ mvetserani, pakuti chiweruzochi chikukhudza inuyo, chifukwa mwakhala msampha+ ku Mizipa ndipo mwakhala ngati ukonde paphiri la Tabori.+
12 “Kulikonse kumene iwo angapite, ndidzawatchera ndi ukonde.+ Ndidzawagwira ngati zolengedwa zouluka m’mlengalenga.+ Ndidzawalanga mogwirizana ndi chenjezo limene ndinauza msonkhano wawo.+