Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 9:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Iye adzaweruza anthu padziko lapansi mwachilungamo.+

      Adzazenga mlandu mitundu ya anthu moyenerera.+

  • Salimo 31:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Ndathawira kwa inu Yehova.+

      Musalole kuti ndichite manyazi.+

      Ndipulumutseni chifukwa cha chilungamo chanu.+

  • Salimo 89:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Chilungamo ndi chiweruzo ndizo maziko a mpando wanu wachifumu.+

      Kukoma mtima kosatha ndi choonadi zili pamaso panu.+

  • Yesaya 26:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Usiku, mtima wanga umakulakalakani.+ Ndithu ndimakufunafunani ndi mtima wonse,+ chifukwa mukadzaweruza dziko lapansi,+ anthu okhala panthaka ya dzikolo adzaphunzira chilungamo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena