Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 29:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kenako Davide anauza mpingo wonse kuti:+ “Tsopano tamandani+ Yehova Mulungu wanu!” Choncho mpingo wonse unayamba kutamanda Yehova Mulungu wa makolo awo, ndipo anagwada+ n’kuwerama mpaka nkhope zawo pansi+ kwa Yehova ndi kwa mfumu.

  • Salimo 34:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Ndidzatamanda Yehova nthawi zonse.+

      Ndidzamutamanda ndi pakamwa panga mosalekeza.+

  • Salimo 72:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Adalitsike Yehova Mulungu, Mulungu wa Isiraeli,+

      Iye yekha amene akuchita ntchito zodabwitsa.+

  • Salimo 113:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Dzina la Yehova lidalitsike,+

      Kuyambira tsopano mpaka kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena