Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 29:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Inu Yehova, ukulu,+ mphamvu,+ kukongola,+ ulemerero,+ ndi ulemu+ ndi zanu, chifukwa zinthu zonse zakumwamba ndi za padziko lapansi ndi zanu.+ Ufumu+ ndi wanu, inu Yehova, ndinunso Wokwezeka monga mutu pa onse.+

  • Yobu 12:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Iye ali ndi nzeru ndi mphamvu.+

      Amapereka malangizo ndipo amamvetsa zinthu.+

  • Salimo 147:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Ambuye wathu ndi wamkulu ndipo ali ndi mphamvu zochuluka.+

      Nzeru zake zilibe malire.+

  • Yeremiya 32:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Inu mumasonyeza anthu masauzande ambiri kukoma mtima kosatha.+ Mumabwezera zolakwa za abambo kwa ana awo.*+ Inu ndinu Mulungu woona, wamkulu+ ndi wamphamvu,+ ndipo dzina lanu+ ndinu Yehova wa makamu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena