Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 12:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Iwo amalankhulana zabodza.+

      Amalankhulana ndi milomo yoshashalika+ komanso ndi mitima iwiri.+

  • Salimo 58:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Oipa akhala opotoka maganizo kuyambira ali m’mimba.+

      Iwo asochera kuyambira ali m’mimba,

      Ndipo amalankhula zabodza.+

  • Salimo 64:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Amaumirira kulankhula zoipa,+

      Amakambirana kuti atchere misampha.+

      Iwo amati: “Angaione ndani?”+

  • Miyambo 12:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Maganizo a anthu olungama ndiwo chilungamo.+ Utsogoleri wa anthu oipa ndi wachinyengo.+

  • Miyambo 12:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Chinyengo chimakhala mumtima mwa anthu okonza chiwembu,+ koma olimbikitsa mtendere amasangalala.+

  • Miyambo 26:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Milomo yonena zabwino mwachiphamaso koma mumtima muli zoipa, ili ngati siliva wokutira phale.+

  • 1 Timoteyo 4:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Zimenezi zidzachitikanso chifukwa cha chinyengo cha anthu olankhula mabodza,+ amene chikumbumtima chawo chili ngati chipsera+ chobwera chifukwa chopsa ndi chitsulo chamoto.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena