Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 2:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 “Monga mmene mbala imachitira manyazi ikagwidwa, anthu a m’nyumba ya Isiraeli nawonso achita manyazi,+ iwowo, mafumu awo, akalonga awo, ansembe awo ndiponso aneneri awo.+

  • Yeremiya 48:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Amowabuwo adzachita manyazi ndi Kemosi,+ monga mmene anthu a m’nyumba ya Isiraeli achitira manyazi ndi Beteli, mzinda umene anali kuudalira.+

  • Ezekieli 36:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Dziwani kuti ine sindidzachita zimenezi chifukwa cha inu,’+ watero Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa. ‘Inu a nyumba ya Isiraeli, chitani manyazi ndi kuona kuti mwanyozeka chifukwa cha njira zanu.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena