Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Ngati ndikanati sindikuopa kusautsidwa ndi mdani,+

      Kuti adani awo angamve molakwa,+

      Kutinso anganene kuti: “Dzanja lathu lapambana,+

      Ndipo si Yehova amene wachita zonsezi.”+

  • Salimo 42:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Odana nane akunditonza kwambiri moti zikungokhala ngati mafupa anga aphwanyidwa,+

      Pakuti anthu akundifunsa tsiku lonse kuti: “Mulungu wako ali kuti?”+

  • Salimo 79:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Musalole kuti anthu a mitundu ina azinena kuti: “Mulungu wawo ali kuti?”+

      Pamene mukubwezera anthu a mitundu inawo chifukwa cha magazi a atumiki anu amene anakhetsedwa,+

      Ife tidzaone ndi maso athu.+

  • Salimo 115:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Musalole kuti mitundu izinena kuti:+

      “Mulungu wawo ali kuti tsopano?”+

  • Mika 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Mdani wanga adzaona zimenezi, ndipo amene anali kunena kuti: “Yehova Mulungu wako ali kuti?”+ adzachita manyazi.+ Maso anga adzamuyang’ana.+ Iye adzakhala malo opondedwapondedwa ngati matope a mumsewu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena