Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 32:41
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 41 Ndikanoladi lupanga langa lonyezimira,+

      Dzanja langa likagwira chiweruzo,+

      Ndidzalipsira adani anga,+

      Ndipo ndidzabwezera chilango kwa odana nane kwambiri.+

  • Salimo 81:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Ndikanagonjetsa adani awo mosavuta,+

      Ndipo ndikanalanga adani awo ndi dzanja langa.+

  • Salimo 97:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Patsogolo pake pakuyaka moto,+

      Ndipo ukupsereza adani ake onse omuzungulira.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena