Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 32:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Pamenepo Mose anakhazika pansi mtima wa Yehova Mulungu wake.+ Iye anati: “N’chifukwa chiyani, inu Yehova, mukufuna kuti mkwiyo wanu+ uyakire anthu anu, amene munawatulutsa m’dziko la Iguputo mwa mphamvu zazikulu ndiponso ndi dzanja lamphamvu?

  • Yeremiya 26:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kodi Hezekiya mfumu ya Yuda ndi anthu onse a mu Yuda anamupha? Kodi iye sanaope Yehova ndi kukhazika pansi mtima wa Yehova?+ Kodi atatero, Yehova sanasinthe maganizo ake pa tsoka limene ananena kuti adzawagwetsera?+ Pamenepatu ife tikudziitanira tsoka lalikulu.+

  • Yoweli 1:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 “Dzimangirireni m’chiuno ndipo dzigugudeni pachifuwa,+ inu ansembe. Lirani mofuula, inu atumiki a paguwa lansembe.+ Lowani, valani ziguduli usiku wonse inu atumiki a Mulungu wanga, pakuti nsembe yambewu+ ndi nsembe yachakumwa zachotsedwa m’nyumba ya Mulungu wanu.+

  • Yoweli 1:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Konzekerani nthawi yosala kudya.+ Itanitsani msonkhano wapadera.+ Sonkhanitsani pamodzi akulu ndi anthu onse okhala m’dzikoli kuti akumane kunyumba ya Yehova Mulungu wanu+ ndipo alirire Yehova kuti awathandize.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena