Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Maliko 14:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ndipo akudya chakudya patebulo, Yesu anati: “Ndithu ndikukuuzani, Mmodzi wa inu, amene akudya+ nane limodzi, andipereka.”+

  • Yohane 6:70
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 70 Pamenepo Yesu anati: “Ine ndinakusankhani inu 12,+ si choncho kodi? Komatu mmodzi wa inu ndi wonenera anzake zoipa.”+

  • Yohane 13:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Atanena zimenezi, Yesu anasautsika mu mzimu, ndipo anachitira umboni kuti: “Ndithudi ndikukuuzani, Mmodzi wa inu andipereka.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena